1Tsoka kwa iwe, iwe wowonongawe,
2Inu Yehova, mutikomere mtima ife;
3Mukatulutsa liwu lanu longa bingu mitundu ya anthu imathawa;
4Zofunkha za ku nkhondo za mitundu ina Aisraeli adzazisonkhanitsa ngati mmene limachitira dzombe.
5Yehova wakwezeka kwambiri pakuti amakhala pamwamba pa zonse
6Iye adzakupatsani mtendere pa nthawi yanu,
7Taonani, anthu awo amphamvu akulira mofuwula mʼmisewu;
8Mʼmisewu yayikulu mulibe anthu,
9Dziko likulira ndipo likunka likutha.
10Yehova akunena kuti, “Tsopano ndidzadzambatuka
11Zolingalira zanu nʼzachabechabe
12Anthu a mitundu ina adzatenthedwa ngati miyala ya njereza;
13Inu amene muli kutali, imvani zimene ndachita;
14Mu mzinda wa Ziyoni anthu ochimwa agwidwa ndi mantha;
15Angathe kuti ndi amene amachita zolungama
16Munthu wotere ndiye adzakhale pa nsanja,
17Nthawi imeneyo maso a ana adzaona mfumu ya maonekedwe wokongola
18Mu mtima mwanu muzidzalingalira zoopsa zinachitika kale zija:
19Simudzawaonanso anthu odzikuza aja,
20Taonani Ziyoni, mzinda wa zikondwerero zachipembedzo chathu;
21Kumeneko Yehova adzaonetsa ulemerero wake
22Pakuti Yehova ndi woweruza wathu,
23Zingwe za sitima zapamadzi za adani athu zamasuka,
24Palibe ndi mmodzi yemwe wokhala mʼZiyoni adzanene kuti, “Ndikudwala”