1Taonani, kudzakhala mfumu ina imene idzalamulira mwachilungamo,
2Munthu aliyense adzakhala ngati pothawirapo mphepo
3Ndipo maso a anthu openya sadzakhalanso otseka,
4Anthu a mtima wopupuluma adzadziwa ndi kuchita zinthu mofatsa,
5Chitsiru sichidzatchedwanso munthu waulemu wake
6Pakuti munthu opusa amayankhula zauchitsiru,
7Munthu woyipa njira zake ndi zoyipanso,
8Koma munthu wolemekezeka amalingaliranso kuchita zinthu zabwino,
9Khalani maso, inu akazi
10Pakapita chaka ndi masiku pangʼono
11Nthunthumirani inu okhala mosatekesekanu;
12Dzigugudeni pachifuwa mwachisoni chifukwa minda yachonde,
13Mʼdziko la anthu anga
14Nyumba yaufumu idzasiyidwa,
15Yehova adzatipatsa mzimu wake,
16Tsono mʼchipululu mudzakhala chiweruzo cholungama
17Mtendere udzakhala chipatso chachilungamo;
18Anthu anga adzakhala mʼmidzi yamtendere,
19Ngakhale nkhalango idzawonongedwa ndi matalala
20inutu mudzakhala odalitsika ndithu.