We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 32

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 31 Yesaya Yesaya 33 →

1Taonani, kudzakhala mfumu ina imene idzalamulira mwachilungamo,

2Munthu aliyense adzakhala ngati pothawirapo mphepo

3Ndipo maso a anthu openya sadzakhalanso otseka,

4Anthu a mtima wopupuluma adzadziwa ndi kuchita zinthu mofatsa,

5Chitsiru sichidzatchedwanso munthu waulemu wake

6Pakuti munthu opusa amayankhula zauchitsiru,

7Munthu woyipa njira zake ndi zoyipanso,

8Koma munthu wolemekezeka amalingaliranso kuchita zinthu zabwino,

9Khalani maso, inu akazi

10Pakapita chaka ndi masiku pangʼono

11Nthunthumirani inu okhala mosatekesekanu;

12Dzigugudeni pachifuwa mwachisoni chifukwa minda yachonde,

13Mʼdziko la anthu anga

14Nyumba yaufumu idzasiyidwa,

15Yehova adzatipatsa mzimu wake,

16Tsono mʼchipululu mudzakhala chiweruzo cholungama

17Mtendere udzakhala chipatso chachilungamo;

18Anthu anga adzakhala mʼmidzi yamtendere,

19Ngakhale nkhalango idzawonongedwa ndi matalala

20inutu mudzakhala odalitsika ndithu.

← Yesaya 31 Yesaya Yesaya 33 →