We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 31

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 30 Yesaya Yesaya 32 →

1Tsoka kwa amene amapita ku Igupto kukapempha chithandizo,

2Komatu Yehovayo ndi wanzeru ndipo angathe kuwononga,

3Aigupto ndi anthu chabe osati Mulungu;

4Zimene Yehova akunena kwa ine ndi izi:

5Monga mbalame zowuluka pamwamba pa zisa zake,

6Inu Aisraeli, bwererani kwa Iye amene munamuwukira kwakukulu.

7Pakuti tsiku limenelo nonsenu mudzataya mafano anu a siliva ndi golide amene mumapanga ndi manja anu auchimo.

8“Aasiriya adzaphedwa ku nkhondo ndi mphamvu osati za munthu.

9Mfumu yawo idzamwalira ndi mantha,

← Yesaya 30 Yesaya Yesaya 32 →