1Tsoka kwa amene amapita ku Igupto kukapempha chithandizo,
2Komatu Yehovayo ndi wanzeru ndipo angathe kuwononga,
3Aigupto ndi anthu chabe osati Mulungu;
4Zimene Yehova akunena kwa ine ndi izi:
5Monga mbalame zowuluka pamwamba pa zisa zake,
6Inu Aisraeli, bwererani kwa Iye amene munamuwukira kwakukulu.
7Pakuti tsiku limenelo nonsenu mudzataya mafano anu a siliva ndi golide amene mumapanga ndi manja anu auchimo.
8“Aasiriya adzaphedwa ku nkhondo ndi mphamvu osati za munthu.
9Mfumu yawo idzamwalira ndi mantha,