1Tsoka kwa iwe, Arieli, Arieli,
2Komatu Ine ndidzathira nkhondo Arieli
3Ine ndidzamanga misasa ya nkhondo kulimbana ndi mzindawo;
4Utagwetsedwa pansi, iwe udzayankhula kuchokera mʼnthaka,
5Koma chigulu cha adani ako chidzasanduka chifwirimbwiti.
6Yehova Wamphamvuzonse adzabwera
7Tsono chigulu chankhondo cha mitundu ina yonse chimene chikulimbana ndi mzinda wa Arieli
8Chidzakhala ngati munthu wanjala wolota akudya,
9Pitirizani kuledzera ndipo mudzakhala opusa.
10Yehova wakugonetsani tulo tofa nato.
11Kwa inu mawu onsewa ali ngati buku lotsekedwa, ndipo ngati lipatsidwa kwa wina wodziwa kuwerenga ndi kunena kuti, “Chonde tawerengani bukuli,” iye adzati, “Sindingathe popeza ndi lomatidwa.”
12Kapena ngati lipatsidwa kwa amene sadziwa kuwerenga ndi kunena kuti, “Chonde werenga bukuli,” iye adzayankha kuti, “Ine sindidziwa kuwerenga.”
13Ambuye akuti,
14Nʼchifukwa chakenso Ine ndidzapitirira
15Tsoka kwa amene amayesetsa
16Inu mumazondotsa zinthu
17Kodi Lebanoni posachedwapa sadzasanduka munda wachonde,
18Tsiku limenelo anthu osamva adzamva mawu a mʼbuku,
19Anthu odzichepetsa adzakhalanso ndi chimwemwe mwa Yehova;
20Koma anthu ankhanza adzazimirira,
21Yehova adzalanga amene amasinjirira munthu kuti apezeke wolakwa,
22Choncho Yehova amene anawombola Abrahamu, akunena kwa zidzukulu za Yakobo kuti,
23Akadzaona ana awo ndi
24Anthu opusa adzapeza nzeru;