1Tsoka ufumu wonyada wa zidakwa za ku Efereimu.
2Taonani, ambuye ali naye wina wamphamvu ndi nyonga.
3Ulamuliro wa atsogoleri oledzera
4Ndipo ulemerero wokongola wa mzinda umene uli ngati duwa
5Tsiku limenelo Yehova Wamphamvuzonse
6Iye adzapereka mtima
7Nawonso awa ali dzandidzandi chifukwa cha vinyo
8Pa matebulo onse pali masanzi okhaokha
9Iwo akuti, “Kodi munthu ameneyu akufuna aphunzitse ndani?
10Akuyesa kumatiphunzitsa pangʼonopangʼono
11Mulungu adzayankhula kwa anthu ake kudzera mwa anthu aziyankhulo zachilendo, ziyankhulo zosamveka bwino.
12anakuwuzani kuti,
13Choncho Yehova adzakuphunzitsani
14Nʼchifukwa chake imvani mawu a Yehova,
15Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa,
16Tsono zimene Ambuye Yehova akunena ndi izi:
17Ntchito zolungama zidzakhala ngati chingwe choyezera maziko ake,
18Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa;
19Ndipo ukadzangofika udzakutengani.
20Mudzakhala ngati munthu wogona pa bedi lalifupi kwambiri kuti sangathe kutambalitsapo miyendo;
21Yehova adzamenya nkhondo monga anachitira ku phiri la Perazimu
22Tsopano lekani kunyoza,
23Tcherani khutu ndipo mumve mawu anga;
24Kodi mlimi wofuna kudzala mbewu amangokhalira kutipula kokhakokha?
25Pamene iye wasalaza mundawo,
26Mulungu wake amamulangiza
27Mawere sapunthira chopunthira cha galeta lopanda mikombero,
28Tirigu ayenera kusinjidwa kuti apangire buledi,
29Izinso zimachokera kwa Yehova Wamphamvuzonse,