We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 28

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 27 Yesaya Yesaya 29 →

1Tsoka ufumu wonyada wa zidakwa za ku Efereimu.

2Taonani, ambuye ali naye wina wamphamvu ndi nyonga.

3Ulamuliro wa atsogoleri oledzera

4Ndipo ulemerero wokongola wa mzinda umene uli ngati duwa

5Tsiku limenelo Yehova Wamphamvuzonse

6Iye adzapereka mtima

7Nawonso awa ali dzandidzandi chifukwa cha vinyo

8Pa matebulo onse pali masanzi okhaokha

9Iwo akuti, “Kodi munthu ameneyu akufuna aphunzitse ndani?

10Akuyesa kumatiphunzitsa pangʼonopangʼono

11Mulungu adzayankhula kwa anthu ake kudzera mwa anthu aziyankhulo zachilendo, ziyankhulo zosamveka bwino.

12anakuwuzani kuti,

13Choncho Yehova adzakuphunzitsani

14Nʼchifukwa chake imvani mawu a Yehova,

15Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa,

16Tsono zimene Ambuye Yehova akunena ndi izi:

17Ntchito zolungama zidzakhala ngati chingwe choyezera maziko ake,

18Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa;

19Ndipo ukadzangofika udzakutengani.

20Mudzakhala ngati munthu wogona pa bedi lalifupi kwambiri kuti sangathe kutambalitsapo miyendo;

21Yehova adzamenya nkhondo monga anachitira ku phiri la Perazimu

22Tsopano lekani kunyoza,

23Tcherani khutu ndipo mumve mawu anga;

24Kodi mlimi wofuna kudzala mbewu amangokhalira kutipula kokhakokha?

25Pamene iye wasalaza mundawo,

26Mulungu wake amamulangiza

27Mawere sapunthira chopunthira cha galeta lopanda mikombero,

28Tirigu ayenera kusinjidwa kuti apangire buledi,

29Izinso zimachokera kwa Yehova Wamphamvuzonse,

← Yesaya 27 Yesaya Yesaya 29 →