We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 27

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 26 Yesaya Yesaya 28 →

1Tsiku limenelo,

2Tsiku limenelo Yehova adzati,

3Ine, Yehova, ndimawuyangʼanira;

4Ine sindinakwiye.

5Koma ngati apo ayi, abweretu kwa Ine adani angawo kuti ndidzawateteze;

6Masiku akubwerawo Yakobo adzazika mizu,

7Kodi Yehova anakantha Israeli

8Yehova mwawalanga powapirikitsa ndi kuwatumiza ku ukapolo,

9Yehova adzakhululuka kulakwa kwa Yakobo.

10Mzinda wamalinga uja wasanduka bwinja,

11Pamene nthambi za mitengoyo zauma, zimathyoka

12Tsiku limenelo Yehova adzasonkhanitsa pamodzi anthu ake mmodzimmodzi kumalo opunthira tirigu, kuchokera ku mtsinje wa Yufurate mpaka ku mtsinje wa ku Igupto.

13Ndipo tsiku limenelo lipenga lalikulu lidzalira. Amene akuzunzika ku Asiriya iwo amene ali ku ukapolo ku Igupto adzabwera ndi kudzalambira Yehova pa phiri lopatulika mu Yerusalemu.

← Yesaya 26 Yesaya Yesaya 28 →