1Tsiku limenelo anthu a mʼdziko la Yuda adzayimba nyimbo iyi.
2Tsekulani zipata za mzinda
3Inu mudzamupatsa munthu
4Mudalireni Yehova mpaka muyaya,
5Iye amatsitsa anthu amene amadziyika pamwamba,
6Mapazi a anthu akuwupondereza,
7Njira ya munthu wolungama ndi yosalaza,
8Inde Yehova, timayenda mʼnjira zanu zolungama,
9Moyo wanga umalakalaka Inu usiku wonse;
10Ngakhale mukomere mtima anthu oyipa,
11Inu Yehova, mwatukula dzanja lanu kuti muwalange,
12Yehova, mumatipatsa mtendere;
13Inu Yehova Mulungu wathu, ngakhale takhala tikulamulidwa ndi ena mʼmalo mwanu,
14Iwo tsopano sadzadzukanso;
15Inu Yehova, mwaukulitsa mtundu wathu;
16Yehova, anthu anu anabwera kwa Inu pamene anali mʼmasautso;
17Monga mayi woyembekezera pamene nthawi yake yobereka yayandikira
18Ife chimodzimodzi tinamva ululu, ngati mayi pa nthawi yobala mwana,
19Koma anthu anu amene anafa adzakhalanso ndi moyo;
20Abale anga, pitani mukalowe mʼnyumba zanu
21Taonani, Yehova akubwera kuchokera kumene amakhala;