We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 26

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 25 Yesaya Yesaya 27 →

1Tsiku limenelo anthu a mʼdziko la Yuda adzayimba nyimbo iyi.

2Tsekulani zipata za mzinda

3Inu mudzamupatsa munthu

4Mudalireni Yehova mpaka muyaya,

5Iye amatsitsa anthu amene amadziyika pamwamba,

6Mapazi a anthu akuwupondereza,

7Njira ya munthu wolungama ndi yosalaza,

8Inde Yehova, timayenda mʼnjira zanu zolungama,

9Moyo wanga umalakalaka Inu usiku wonse;

10Ngakhale mukomere mtima anthu oyipa,

11Inu Yehova, mwatukula dzanja lanu kuti muwalange,

12Yehova, mumatipatsa mtendere;

13Inu Yehova Mulungu wathu, ngakhale takhala tikulamulidwa ndi ena mʼmalo mwanu,

14Iwo tsopano sadzadzukanso;

15Inu Yehova, mwaukulitsa mtundu wathu;

16Yehova, anthu anu anabwera kwa Inu pamene anali mʼmasautso;

17Monga mayi woyembekezera pamene nthawi yake yobereka yayandikira

18Ife chimodzimodzi tinamva ululu, ngati mayi pa nthawi yobala mwana,

19Koma anthu anu amene anafa adzakhalanso ndi moyo;

20Abale anga, pitani mukalowe mʼnyumba zanu

21Taonani, Yehova akubwera kuchokera kumene amakhala;

← Yesaya 25 Yesaya Yesaya 27 →