1Yehova ndinu Mulungu wanga;
2Inu mwasandutsa mzinda uja kukhala mulu wamiyala.
3Nʼchifukwa chake anthu amphamvu adzakulemekezani;
4Inu mwakhala ngati populumukira pa anthu osauka,
5ndiponso ngati kutentha mʼdziko lowuma.
6Pa phiri ili Yehova Wamphamvuzonse adzakonzera
7Iye adzachotsa kulira
8Yehova adzathetsa imfa mpaka muyaya,
9Tsiku limenelo iwo adzati,
10Yehova adzateteza phiri limeneli ndi dzanja lake;
11Amowabuwo adzatambasula manja awo mʼmenemo,
12Iye adzagumula malinga awo ataliatali