We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 25

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 24 Yesaya Yesaya 26 →

1Yehova ndinu Mulungu wanga;

2Inu mwasandutsa mzinda uja kukhala mulu wamiyala.

3Nʼchifukwa chake anthu amphamvu adzakulemekezani;

4Inu mwakhala ngati populumukira pa anthu osauka,

5ndiponso ngati kutentha mʼdziko lowuma.

6Pa phiri ili Yehova Wamphamvuzonse adzakonzera

7Iye adzachotsa kulira

8Yehova adzathetsa imfa mpaka muyaya,

9Tsiku limenelo iwo adzati,

10Yehova adzateteza phiri limeneli ndi dzanja lake;

11Amowabuwo adzatambasula manja awo mʼmenemo,

12Iye adzagumula malinga awo ataliatali

← Yesaya 24 Yesaya Yesaya 26 →