1Taonani, Yehova adzawononga dziko lapansi
2Aliyense zidzamuchitikira mofanana:
3Dziko lapansi lidzawonongedwa kwathunthu
4Dziko lapansi likulira ndipo likufota,
5Anthu ayipitsa dziko lapansi;
6Nʼchifukwa chake matemberero akuwononga dziko lapansi;
7Vinyo watsopano watha ndipo mphesa zikufota;
8Kulira kokometsera kwa matambolini kwatha,
9Anthu sadzayimbanso akumwa vinyo;
10Mzinda wachisokonezo uja wawonongeka;
11Anthu akulira mʼmisewu kufuna vinyo;
12Mzinda wasanduka bwinja
13Zimenezi ndizo zidzachitikire mitundu yonse ya dziko lapansi
14Koma otsala onse akufuwula ndi kuyimba mwachimwemwe;
15Nʼchifukwa chake inu akummawa, tamandani Yehova;
16Kuchokera kumalekezero a dziko lapansi tikumva kuyimba kotamanda
17Inu anthu adziko lapansi, zoopsa, dzenje
18Aliyense wothawa phokoso la zoopsa
19Dziko lapansi lathyokathyoka,
20Dziko lapansi likudzandira ngati munthu woledzera
21Tsiku limenelo Yehova adzalanga
22Mulungu adzawasonkhanitsa pamodzi
23Mwezi udzanyazitsidwa, dzuwa lidzachita manyazi;