We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 24

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 23 Yesaya Yesaya 25 →

1Taonani, Yehova adzawononga dziko lapansi

2Aliyense zidzamuchitikira mofanana:

3Dziko lapansi lidzawonongedwa kwathunthu

4Dziko lapansi likulira ndipo likufota,

5Anthu ayipitsa dziko lapansi;

6Nʼchifukwa chake matemberero akuwononga dziko lapansi;

7Vinyo watsopano watha ndipo mphesa zikufota;

8Kulira kokometsera kwa matambolini kwatha,

9Anthu sadzayimbanso akumwa vinyo;

10Mzinda wachisokonezo uja wawonongeka;

11Anthu akulira mʼmisewu kufuna vinyo;

12Mzinda wasanduka bwinja

13Zimenezi ndizo zidzachitikire mitundu yonse ya dziko lapansi

14Koma otsala onse akufuwula ndi kuyimba mwachimwemwe;

15Nʼchifukwa chake inu akummawa, tamandani Yehova;

16Kuchokera kumalekezero a dziko lapansi tikumva kuyimba kotamanda

17Inu anthu adziko lapansi, zoopsa, dzenje

18Aliyense wothawa phokoso la zoopsa

19Dziko lapansi lathyokathyoka,

20Dziko lapansi likudzandira ngati munthu woledzera

21Tsiku limenelo Yehova adzalanga

22Mulungu adzawasonkhanitsa pamodzi

23Mwezi udzanyazitsidwa, dzuwa lidzachita manyazi;

← Yesaya 23 Yesaya Yesaya 25 →