1Uthenga wonena za Turo:
2Khalani chete inu anthu okhala mʼmbali mwa nyanja,
3Pa nyanja zazikulu
4Chita manyazi, iwe Sidimu
5Mawuwa akadzamveka ku Igupto,
6Wolokerani ku Tarisisi,
7Kodi uwu si mzinda wachisangalalo uja,
8Kodi ndani anakonza zimenezi kuti zigwere Turo, mzinda umene unakhazikitsa mizinda ina,
9Yehova Wamphamvuzonse anakonza zimenezi
10Mubalalike mʼdziko mwanu ngati mtsinje wa Nailo
11Yehova watambasula dzanja lake kuloza ku nyanja
12Iye anati, “Simudzakondwanso konse,
13Onani dziko la Ababuloni,
14Lirani mofuwula, inu anthu oyendetsa sitima za pa madzi za ku Tarisisi;
15Pa nthawi imeneyo Turo adzayiwalika pa zaka 70, amene ndi masiku a moyo wa mfumu. Koma potsiriza pa zaka 70 zimenezi, Turo adzakhala ngati mkazi wachiwerewere woyimbidwa mu nyimbo:
16“Tenga zeze wako uzungulire mzinda,
17Pakutha pa zaka 70, Yehova adzachitapo kanthu pa Turo. Iye adzabwerera ku ntchito yake yakale monga mkazi wachiwerewere ndipo adzachita zachiwerewere ndi maufumu onse a dziko lapansi.
18Koma phindu lake ndi malipiro ake adzazipereka kwa Yehova; sadzazikundika kapena kuzisunga. Phindu lake lidzapita kwa mtumiki wa Yehova kuti agule zakudya zambiri ndi zovala zokongola.