We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 2

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 1 Yesaya Yesaya 3 →

1Nazi zinthu zokhudza Yuda ndi Yerusalemu, zimene Yesaya mwana wa Amozi anaziona mʼmasomphenya:

2Mʼmasiku otsiriza,

3Anthu ambiri adzabwera ndikunena kuti,

4Iye adzaweruza pakati pa mayiko,

5Inu nyumba ya Yakobo, bwerani,

6Inu Yehova mwawakana anthu anu,

7Dziko lawo ndi lodzaza ndi siliva ndi golide;

8Dziko lawo ndi lodzaza ndi mafano;

9Tsono munthu aliyense adzachepetsedwa

10Lowani mʼmatanthwe,

11Kudzikuza kwa anthu kudzatha,

12Yehova Wamphamvuzonse wakonzeratu tsiku

13tsiku la mikungudza yonse ya ku Lebanoni, yayitali ndi yoonekera patali,

14tsiku la mapiri onse ataliatali

15tsiku la nsanja zonse zazitali

16tsiku la sitima zapamadzi zonse za ku Tarisisi

17Kudzikuza kwa munthu kudzatha

18ndipo mafano onse adzatheratu.

19Anthu adzathawira mʼmapanga a matanthwe

20Tsiku limenelo anthu adzatayira

21Adzathawira mʼmapanga a matanthwe

22Lekani kudalira munthu,

← Yesaya 1 Yesaya Yesaya 3 →