1Nazi zinthu zokhudza Yuda ndi Yerusalemu, zimene Yesaya mwana wa Amozi anaziona mʼmasomphenya:
2Mʼmasiku otsiriza,
3Anthu ambiri adzabwera ndikunena kuti,
4Iye adzaweruza pakati pa mayiko,
5Inu nyumba ya Yakobo, bwerani,
6Inu Yehova mwawakana anthu anu,
7Dziko lawo ndi lodzaza ndi siliva ndi golide;
8Dziko lawo ndi lodzaza ndi mafano;
9Tsono munthu aliyense adzachepetsedwa
10Lowani mʼmatanthwe,
11Kudzikuza kwa anthu kudzatha,
12Yehova Wamphamvuzonse wakonzeratu tsiku
13tsiku la mikungudza yonse ya ku Lebanoni, yayitali ndi yoonekera patali,
14tsiku la mapiri onse ataliatali
15tsiku la nsanja zonse zazitali
16tsiku la sitima zapamadzi zonse za ku Tarisisi
17Kudzikuza kwa munthu kudzatha
18ndipo mafano onse adzatheratu.
19Anthu adzathawira mʼmapanga a matanthwe
20Tsiku limenelo anthu adzatayira
21Adzathawira mʼmapanga a matanthwe
22Lekani kudalira munthu,