We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 3

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 2 Yesaya Yesaya 4 →

1Taonani tsopano, Ambuye

2anthu amphamvu ndi asilikali ankhondo,

3atsogoleri a ankhondo makumi asanu ndi anthu olemekezeka,

4Ndidzawayikira anyamata kuti akhale mafumu awo;

5Anthu adzazunzana,

6Munthu adzagwira mʼbale wake

7Koma tsiku limenelo mʼbale wakeyo adzafuwula kuti,

8Yerusalemu akudzandira,

9Maonekedwe a nkhope zawo amawatsutsa;

10Nena kwa olungama kuti zonse zidzawayendera bwino,

11Tsoka kwa anthu oyipa! Mavuto ali pa iwo!

12Achinyamata akupondereza anthu anga,

13Yehova wakhala pamalo pake mʼbwalo la milandu;

14Yehova akuwazenga milandu

15Nʼchifukwa chiyani inu mukupsinja anthu anga,

16Yehova akunena kuti,

17Nʼchifukwa chake Ambuye, adzatulutsa zipere pa mitu ya akazi a ku Ziyoniwo;

18Tsiku limenelo Ambuye adzawachotsera zodzikongoletsera zawo: za mʼmiyendo, za ku mutu za mʼkhosi,

19ndolo ndi zibangiri, nsalu zophimba pa nkhope,

20maduku, zigwinjiri za mʼmiyendo ndi malamba, mabotolo a zonunkhira ndi zithumwa,

21mphete ndi zipini,

22zovala za pa mphwando, zipewa ndi mwinjiro, zikwama,

23magalasi oyangʼanira, zovala zosalala, nduwira ndiponso nsalu za mʼmapewa.

24Mʼmalo mwa kununkhira azidzanunkha,

25Iwe Yerusalemu anthu ako aamuna adzaphedwa ndi lupanga,

26Pa zipata za Ziyoni padzakhala kubuma ndi kulira;

← Yesaya 2 Yesaya Yesaya 4 →