We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

Yesaya Yesaya 2 →

1Masomphenya wonena za Yuda ndi Yerusalemu, amene Yesaya mwana wa Amozi, anaona pa nthawi ya ulamuliro wa Uziya, Yotamu, Ahazi ndi Hezekiya, mafumu a Yuda.

2Tamverani, miyamba inu! Tchera khutu, iwe dziko lapansi!

3Ngʼombe imadziwa mwini wake,

4Haa, mtundu wochimwa,

5Chifukwa chiyani mukufuna kuti muzingolangidwabe?

6Kuchokera ku phazi mpaka ku mutu

7Dziko lanu lasanduka bwinja,

8Mwana wamkazi wa Ziyoni watsala yekha

9Yehova Wamphamvuzonse akanapanda

10Imvani mawu a Yehova,

11Yehova akuti, “Kodi ndili nazo chiyani

12Ndani anakulamulirani kuti

13Siyani kubweretsa nsembe zachabechabezo!

14Zikondwerero zanu za Mwezi Watsopano ndi masiku anu opatulika

15Mukamatambasula manja anu popemphera,

16sambani, dziyeretseni.

17phunzirani kuchita zabwino!

18Yehova akuti,

19Ngati muli okonzeka kundimvera

20koma mukakana ndi kuwukira

21Taonani momwe mzinda wokhulupirika

22Siliva wako wasanduka wachabechabe,

23Atsogoleri ako ndi owukira,

24Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova Wamphamvu,

25Ndidzatambasula dzanja langa kuti ndilimbane nawe;

26Ndidzabwezeretsa oweruza ako ngati masiku amakedzana,

27Ziyoni adzawomboledwa mwa chiweruzo cholungama,

28Koma owukira ndi ochimwa adzawawonongera pamodzi,

29“Mudzachita nayo manyazi mitengo ya thundu

30Mudzakhala ngati mtengo wa thundu umene masamba ake akufota,

31Munthu wamphamvu adzasanduka ngati udzu wowuma,

Yesaya Yesaya 2 →