1Masomphenya wonena za Yuda ndi Yerusalemu, amene Yesaya mwana wa Amozi, anaona pa nthawi ya ulamuliro wa Uziya, Yotamu, Ahazi ndi Hezekiya, mafumu a Yuda.
2Tamverani, miyamba inu! Tchera khutu, iwe dziko lapansi!
3Ngʼombe imadziwa mwini wake,
4Haa, mtundu wochimwa,
5Chifukwa chiyani mukufuna kuti muzingolangidwabe?
6Kuchokera ku phazi mpaka ku mutu
7Dziko lanu lasanduka bwinja,
8Mwana wamkazi wa Ziyoni watsala yekha
9Yehova Wamphamvuzonse akanapanda
10Imvani mawu a Yehova,
11Yehova akuti, “Kodi ndili nazo chiyani
12Ndani anakulamulirani kuti
13Siyani kubweretsa nsembe zachabechabezo!
14Zikondwerero zanu za Mwezi Watsopano ndi masiku anu opatulika
15Mukamatambasula manja anu popemphera,
16sambani, dziyeretseni.
17phunzirani kuchita zabwino!
18Yehova akuti,
19Ngati muli okonzeka kundimvera
20koma mukakana ndi kuwukira
21Taonani momwe mzinda wokhulupirika
22Siliva wako wasanduka wachabechabe,
23Atsogoleri ako ndi owukira,
24Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova Wamphamvu,
25Ndidzatambasula dzanja langa kuti ndilimbane nawe;
26Ndidzabwezeretsa oweruza ako ngati masiku amakedzana,
27Ziyoni adzawomboledwa mwa chiweruzo cholungama,
28Koma owukira ndi ochimwa adzawawonongera pamodzi,
29“Mudzachita nayo manyazi mitengo ya thundu
30Mudzakhala ngati mtengo wa thundu umene masamba ake akufota,
31Munthu wamphamvu adzasanduka ngati udzu wowuma,