1Tsoka kwa anthu a ku Kusi.
2Dziko limenelo limatumiza akazembe pa mtsinje wa Nailo,
3Inu nonse anthu a pa dziko lonse,
4Pakuti Yehova akunena kwa ine kuti,
5Pakuti, anthu asanayambe kukolola, maluwa atayoyoka
6Mitembo ya anthu ankhondo adzasiyira mbalame zamʼmapiri zodya nyama
7Pa nthawi imeneyo anthu adzabwera ndi mphatso kwa Yehova Wamphamvuzonse,