We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 17

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 16 Yesaya Yesaya 18 →

1Uthenga wonena za Damasiko:

2Mizinda ya Aroeri idzakhala yopanda anthu

3Ku Efereimu sikudzakhalanso linga,

4“Tsiku limenelo ulemerero wa Yakobo udzazimirira;

5Israeli adzakhala ngati munda wa tirigu

6Komabe Aisraeli ochepa okha ndiwo ati adzatsale

7Tsiku limenelo anthu adzayangʼana Mlengi wawo

8Iwo sadzakhulupiriranso maguwa ansembe,

9Tsiku limenelo mizinda yawo yamphamvu, imene anasiya chifukwa cha Aisraeli, idzakhala ngati malo osiyidwa kuti awirire ndi kumera ziyangoyango. Ndipo yonse idzakhala mabwinja.

10Inu mwayiwalatu Mulungu Mpulumutsi wanu;

11nimuyembekeza kuti zikule tsiku lomwelo

12Aa, mkokomo wa anthu a mitundu yambiri,

13Ngakhale ankhondo a mitundu ina akubwera ndi mkokomo ngati wa madzi ambiri,

14Pofika nthawi yamadzulo zoopsa zidzayamba kuchitika,

← Yesaya 16 Yesaya Yesaya 18 →