1Uthenga wonena za Damasiko:
2Mizinda ya Aroeri idzakhala yopanda anthu
3Ku Efereimu sikudzakhalanso linga,
4“Tsiku limenelo ulemerero wa Yakobo udzazimirira;
5Israeli adzakhala ngati munda wa tirigu
6Komabe Aisraeli ochepa okha ndiwo ati adzatsale
7Tsiku limenelo anthu adzayangʼana Mlengi wawo
8Iwo sadzakhulupiriranso maguwa ansembe,
9Tsiku limenelo mizinda yawo yamphamvu, imene anasiya chifukwa cha Aisraeli, idzakhala ngati malo osiyidwa kuti awirire ndi kumera ziyangoyango. Ndipo yonse idzakhala mabwinja.
10Inu mwayiwalatu Mulungu Mpulumutsi wanu;
11nimuyembekeza kuti zikule tsiku lomwelo
12Aa, mkokomo wa anthu a mitundu yambiri,
13Ngakhale ankhondo a mitundu ina akubwera ndi mkokomo ngati wa madzi ambiri,
14Pofika nthawi yamadzulo zoopsa zidzayamba kuchitika,