1Uthenga wonena za Mowabu:
2Anthu a ku Diboni akupita ku nyumba ya milungu yawo,
3Mʼmisewu akuvala ziguduli;
4Anthu a ku Hesiboni ndi Eleali akulira mofuwula,
5Inenso ndikulirira Mowabu;
6Madzi a ku Nimurimu aphwa
7Kotero kuti chuma chomwe anachipeza ndi kuchisunga,
8Kulira kwawo kukumveka mʼdziko lonse la Mowabu;
9Madzi a ku Dimoni afiira ndi magazi,