We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 15

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 14 Yesaya Yesaya 16 →

1Uthenga wonena za Mowabu:

2Anthu a ku Diboni akupita ku nyumba ya milungu yawo,

3Mʼmisewu akuvala ziguduli;

4Anthu a ku Hesiboni ndi Eleali akulira mofuwula,

5Inenso ndikulirira Mowabu;

6Madzi a ku Nimurimu aphwa

7Kotero kuti chuma chomwe anachipeza ndi kuchisunga,

8Kulira kwawo kukumveka mʼdziko lonse la Mowabu;

9Madzi a ku Dimoni afiira ndi magazi,

← Yesaya 14 Yesaya Yesaya 16 →