1Yehova adzachitira chifundo Yakobo;
2Anthu a mitundu ina adzaperekeza a Israeli
3Yehova akadzakupumitsani ku zowawa ndi mavuto, ndiponso kuntchito yakalavulagaga imene ankakugwiritsani,
4mudzayankhula monyogodola mfumu ya Babuloni kuti,
5Yehova wathyola chikwapu cha anthu oyipa,
6Mfumu ya ku Babuloni inkakantha mitundu ya anthu mwaukali
7Koma tsopano mayiko onse ali pa mpumulo ndi pa mtendere;
8Ngakhale mitengo ya payini ndi mikungudza ya ku Lebanoni
9Ku manda kwatekeseka
10Onse adzayankha;
11Ulemerero wako wonse walowa mʼmanda,
12Wagwa pansi bwanji kuchoka kumwamba,
13Mu mtima mwako unkanena kuti,
14Ndidzakwera pamwamba pa mitambo;
15Koma watsitsidwa mʼmanda
16Anthu akufa adzakupenyetsetsa
17munthu amene anasandutsa dziko lonse chipululu,
18Mafumu onse a mitundu ya anthu akugona mwaulemu
19Koma iwe watayidwa kunja kwa manda ako,
20Sudzayikidwa nawo mʼmanda mwaulemu,
21Konzani malo woti muphere ana ake aamuna
22Yehova Wamphamvuzonse akuti,
23“Ndidzawusandutsa mzindawo malo okhalamo anungu
24Yehova Wamphamvuzonse walumbira kuti,
25Ndidzawawononga Asiriya mʼdziko langa;
26Izi ndizo ndakonza kuti zichitike pa dziko lonse lapansi,
27Pakuti Yehova Wamphamvuzonse watsimikiza, ndipo ndani angamuletse?
28Uthenga uwu unabwera chaka chimene mfumu Ahazi anamwalira:
29Musakondwere inu Afilisti nonse
30Osaukitsitsa adzapeza chakudya
31Lirani kwambiri, anthu a pa chipata! Fuwulani kwambiri, anthu a mu mzinda!
32Kodi tidzawayankha chiyani