We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 14

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 13 Yesaya Yesaya 15 →

1Yehova adzachitira chifundo Yakobo;

2Anthu a mitundu ina adzaperekeza a Israeli

3Yehova akadzakupumitsani ku zowawa ndi mavuto, ndiponso kuntchito yakalavulagaga imene ankakugwiritsani,

4mudzayankhula monyogodola mfumu ya Babuloni kuti,

5Yehova wathyola chikwapu cha anthu oyipa,

6Mfumu ya ku Babuloni inkakantha mitundu ya anthu mwaukali

7Koma tsopano mayiko onse ali pa mpumulo ndi pa mtendere;

8Ngakhale mitengo ya payini ndi mikungudza ya ku Lebanoni

9Ku manda kwatekeseka

10Onse adzayankha;

11Ulemerero wako wonse walowa mʼmanda,

12Wagwa pansi bwanji kuchoka kumwamba,

13Mu mtima mwako unkanena kuti,

14Ndidzakwera pamwamba pa mitambo;

15Koma watsitsidwa mʼmanda

16Anthu akufa adzakupenyetsetsa

17munthu amene anasandutsa dziko lonse chipululu,

18Mafumu onse a mitundu ya anthu akugona mwaulemu

19Koma iwe watayidwa kunja kwa manda ako,

20Sudzayikidwa nawo mʼmanda mwaulemu,

21Konzani malo woti muphere ana ake aamuna

22Yehova Wamphamvuzonse akuti,

23“Ndidzawusandutsa mzindawo malo okhalamo anungu

24Yehova Wamphamvuzonse walumbira kuti,

25Ndidzawawononga Asiriya mʼdziko langa;

26Izi ndizo ndakonza kuti zichitike pa dziko lonse lapansi,

27Pakuti Yehova Wamphamvuzonse watsimikiza, ndipo ndani angamuletse?

28Uthenga uwu unabwera chaka chimene mfumu Ahazi anamwalira:

29Musakondwere inu Afilisti nonse

30Osaukitsitsa adzapeza chakudya

31Lirani kwambiri, anthu a pa chipata! Fuwulani kwambiri, anthu a mu mzinda!

32Kodi tidzawayankha chiyani

← Yesaya 13 Yesaya Yesaya 15 →