1Uthenga onena za Babuloni umene Yesaya mwana wa Amozi anawulandira:
2Kwezani mbendera yankhondo pa phiri loti see,
3Ine Yehova, ndalamulira ankhondo anga;
4Tamvani phokoso ku mapiri,
5Iwo akuchokera ku mayiko akutali,
6Lirani mofuwula, pakuti tsiku la Yehova layandikira;
7Zimenezi zinafowoketsa manja onse,
8Anthu adzagwidwa ndi mantha aakulu,
9Taonani, tsiku la Yehova likubwera,
10Nyenyezi zakumwamba ndiponso zonse zamlengalenga
11Ndidzalanga dziko lonse chifukwa cha zolakwa zake,
12Ndidzasandutsa anthu kukhala ovuta kupeza kuposa mmene amasowera golide wabwino.
13Tsono ndidzagwedeza miyamba
14Ngati mbawala zosakidwa,
15Aliyense amene atadzapezeke ndi kugwidwa
16Ana awo akhanda adzaphwanyidwa iwo akuona;
17Taona, Ine ndidzadzutsa Amedi amene safuna siliva
18Adzapha anyamata ndi mauta awo;
19Babuloni, ufumu wake ndi waulemerero kuposa mafumu onse.
20Anthu sadzakhalamonso
21Koma nyama zakuthengo ndizo zidzakhale kumeneko,
22Mu nsanja zake muzidzalira afisi,