We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Habakuku 2

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Habakuku 1 Habakuku Habakuku 3 →

1Ndidzakhala pa malo anga aulonda,

2Tsono Yehova anandiyankha, nati:

3Pakuti masomphenyawa akudikira nthawi yake;

4“Taona, mdani wadzitukumula;

5Ndithu, wasokonezeka ndi vinyo;

6“Kodi onse ogwidwawo sadzamunyoza ndi kumunyogodola ponena kuti,

7Kodi angongole ako sadzakuwukira mwadzidzidzi?

8Pakuti unafunkha mitundu yambiri ya anthu,

9“Tsoka kwa amene amalemera ndi chuma chochipeza mwachinyengo,

10Wakonzekera kuwononga mitundu yambiri ya anthu,

11Mwala pa khoma udzafuwula,

12“Tsoka kwa amene amanga mzinda pokhetsa magazi

13Kodi Yehova Wamphamvuzonse sanatsimikize

14Pakuti dziko lapansi lidzadzaza ndi chidziwitso cha ulemerero wa Yehova,

15“Tsoka kwa amene amamwetsa anzake zakumwa zoledzeretsa,

16Udzachita manyazi mʼmalo mokhala ndi ulemerero.

17Udzathedwa nzeru ndi chiwawa chimene unachita ku Lebanoni,

18“Kodi fano lili ndi phindu lanji, poti analisema ndi munthu,

19Tsoka kwa amene amawuza mtengo kuti, ‘Khala wamoyo!’

20Koma Yehova ali mʼNyumba yake yopatulika;

← Habakuku 1 Habakuku Habakuku 3 →