We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Habakuku 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

Habakuku Habakuku 2 →

1Uthenga umene mneneri Habakuku analandira mʼmasomphenya.

2Kodi inu Yehova, ndidzakhala ndikukupemphani thandizo kwa nthawi yayitali motani,

3Chifukwa chiyani mukundionetsa zinthu zoyipa?

4Kotero malamulo anu atha mphamvu,

5“Yangʼanani pakati pa mitundu ya anthu, ndipo penyetsetsani,

6Pakuti taonani, Ine ndikuwutsa Ababuloni,

7Iwowa ndi anthu ochititsa mantha, ndipo ndi owopsa;

8Akavalo awo ndi aliwiro kwambiri kupambana akambuku

9onse akubwera atakonzekera zachiwawa.

10Akunyoza mafumu

11Kenaka amasesa mofulumira ngati mphepo nʼkumangopitirirabe,

12Inu Yehova, kodi sindinu wachikhalire?

13Maso anu ndi oyera kwambiri safuna kuona choyipa;

14Mwasandutsa anthu kukhala ngati nsomba zamʼnyanja,

15Mdani wawo woyipa amakoka anthu onse ndi mbedza,

16Choncho iye amaperekera nsembe ukonde wake

17Kodi iye azipitirabe kugwiritsa ntchito makoka akewo,

Habakuku Habakuku 2 →