We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Habakuku 3

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Habakuku 2 Habakuku

1Pemphero la mneneri Habakuku potsata mayimbidwe a Sigionoti.

2Inu Yehova, ndamva za kutchuka kwanu;

3Mulungu anabwera kuchokera ku Temani,

4Kuwala kwa ulemerero wake kunali ngati kutuluka kwa dzuwa;

5Patsogolo pake pankagwa mliri;

6Iye anayimirira ndi kugwedeza dziko lapansi;

7Ndinaona matenti a ku Kusani ali pa mavuto,

8Inu Yehova, kodi munakwiyira mitsinje?

9Munasolola uta wanu mʼchimake,

10mapiri anakuonani ndipo anagwedezeka.

11Dzuwa ndi mwezi zinayima chilili mlengalenga,

12Munayendayenda mʼdziko lapansi muli ndi ukali,

13Munapita kukalanditsa anthu anu,

14Ndi mkondo wake womwe munalasa mtsogoleri wake

15Munapondaponda pa nyanja ndi akavalo anu,

16Ndinamva ndipo mtima wanga unagunda kwambiri,

17Ngakhale mtengo wa mkuyu usachite maluwa,

18komabe ine ndidzakondwera mwa Yehova,

19Ambuye Yehova ndiye mphamvu yanga;

← Habakuku 2 Habakuku