1Ponya chakudya chako pa madzi,
2Ndalama zako uzisungitse kwa anthu asanu ndi awiri, inde kwa anthu asanu ndi atatu,
3Ngati mitambo yadzaza ndi madzi,
4Amene amayangʼana mphepo sadzadzala;
5Momwe sudziwira mayendedwe a mphepo,
6Dzala mbewu zako mmawa
7Kuwala nʼkwabwino,
8Munthu akakhala wa zaka zambiri,
9Kondwera mnyamata iwe, pamene ukanali wamngʼono,
10Choncho uchotse zokusautsa mu mtima mwako,