We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Mlaliki 11

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Mlaliki 10 Mlaliki Mlaliki 12 →

1Ponya chakudya chako pa madzi,

2Ndalama zako uzisungitse kwa anthu asanu ndi awiri, inde kwa anthu asanu ndi atatu,

3Ngati mitambo yadzaza ndi madzi,

4Amene amayangʼana mphepo sadzadzala;

5Momwe sudziwira mayendedwe a mphepo,

6Dzala mbewu zako mmawa

7Kuwala nʼkwabwino,

8Munthu akakhala wa zaka zambiri,

9Kondwera mnyamata iwe, pamene ukanali wamngʼono,

10Choncho uchotse zokusautsa mu mtima mwako,

← Mlaliki 10 Mlaliki Mlaliki 12 →