We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Mlaliki 10

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Mlaliki 9 Mlaliki Mlaliki 11 →

1Monga ntchentche zakufa zimayika fungo loyipa mʼmafuta onunkhira,

2Mtima wa munthu wanzeru umamutsogolera bwino,

3Chitsiru ngakhale chikamayenda mu msewu,

4Ngati wolamulira akukwiyira,

5Pali choyipa chimene ndinachiona pansi pano,

6Zitsiru amazipatsa ntchito zambiri zapamwamba,

7Ndaona akapolo atakwera pa akavalo,

8Amene amakumba dzenje adzagwamo yekha;

9Amene amaphwanya miyala adzapwetekedwa ndi miyalayo;

10Ngati nkhwangwa ili yobuntha

11Nʼkopanda phindu kudziwa kuseweretsa njoka

12Mawu a pakamwa pa munthu wanzeru ndi okondweretsa,

13Chitsiru chimayamba ndi mawu opusa;

14ndipo chitsiru chimachulukitsa mawu.

15Chitsiru chimatopa msanga ndi ntchito yochepa;

16Tsoka kwa iwe, iwe dziko ngati mfumu yako ikali mwana,

17Wodala iwe, iwe dziko ngati mfumu yako ndi mwana wolemekezeka

18Ngati munthu ndi waulesi, denga lake limaloshoka;

19Phwando ndi lokondweretsa anthu,

20Usanyoze mfumu ngakhale mu mtima mwako,

← Mlaliki 9 Mlaliki Mlaliki 11 →