1Iwe wokongola kuposa akazi onsewa,
2Wachikondi wanga watsikira ku munda kwake,
3Wokondedwa wangayo ndine wake ndipo iyeyo ndi wangawanga;
4Ndiwe wokongola, bwenzi langa, ngati Tiriza,
5Usandipenyetsetse;
6Mano ako ali ngati gulu la nkhosa
7Kukhalira kumbuyo kwa nsalu yako yophimba kumutu,
8Ngakhale patakhala akazi a mfumu 60,
9koma nkhunda yanga, wangwiro wanga ndi wosiyana ndi wina aliyense;
10Ndani uyu akuoneka ngati mʼbandakucha,
11Ndinatsikira ku munda wa mitengo ya alimondi
12Ndisanazindikire kanthu,
13Bwerera, bwerera iwe namwali wa ku Sulami;