1Ndalowa mʼmunda mwanga, iwe mlongo wanga, iwe mkwatibwi wanga;
2Ndinagona tulo koma mtima wanga unali maso.
3Ndavula kale zovala zanga,
4Bwenzi langa anapisa dzanja lake pa chibowo cha pa chitseko;
5Ndinanyamuka kukamutsekulira wachikondi wangayo,
6Ndinamutsekulira wachikondi wanga,
7Alonda anandipeza
8Inu akazi a ku Yerusalemu ndithu ndikukupemphani,
9Iwe wokongola kuposa akazi onsewa,
10Wokondedwa wangayo ndi wowala kwambiri ndi wathanzi
11Mutu wake ndi golide woyengeka bwino;
12Maso ake ali ngati nkhunda
13Masaya ake ali ngati timinda ta mbewu zokometsera zakudya
14Manja ake ali ngati ndodo zagolide
15Miyendo yake ili ngati mizati yamwala,
16Milomo yake ndi yosangalatsa kwambiri;