We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Nyimbo ya Solomoni 4

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Nyimbo ya Solomoni 3 Nyimbo ya Solomoni Nyimbo ya Solomoni 5 →

1Ndiwe wokongoladi wokondedwa wanga!

2Mano ako ali ngati gulu la nkhosa zomwe zangometedwa kumene,

3Milomo yako ili ngati mbota yofiira;

4Khosi lako lili ngati nsanja ya Davide,

5Mawere ako ali ngati tiana tiwiri ta nswala,

6Kamphepo kamadzulo kakayamba kuwuzira

7Ndiwe wokongola kwambiri wokondedwa wanga;

8Tiye tichoke ku Lebanoni iwe mkwatibwi wanga,

9Iwe mlongo wanga, mkwatibwi wanga, wanditenga mtima,

10Iwe mlongo wanga, mkwatibwi wanga, chikondi chako nʼchosangalatsa!

11Iwe mkwatibwi wanga, milomo yako ikuchucha uchi ngati chisa cha njuchi;

12Iwe mlongo wanga, mkwatibwi wanga, ndiwe munda wopiringidzidwa;

13Zomera zako ndi munda wa zipatso za makangadza;

14nadi ndi safiro,

15Iwe ndiwe kasupe wa mʼmunda,

16Dzuka, iwe mphepo yakumpoto,

← Nyimbo ya Solomoni 3 Nyimbo ya Solomoni Nyimbo ya Solomoni 5 →