1Yehova akuti,
2Ine ndidzatumiza moto pa Mowabu,
3Ndidzawononga wolamulira wake
4Yehova akuti,
5Ine ndidzatumiza moto pa Yuda,
6Yehova akuti,
7Amapondereza anthu osauka
8Anthuwo amakagonana mʼmbali mwa guwa lililonse la nsembe
9“Ine ndinawononga Aamori pamaso pawo,
10“Ine ndinakutulutsani ku Igupto,
11Ine ndinawutsanso ena mwa ana ako kuti akhale aneneri,
12“Koma inu munawamwetsa vinyo anaziri aja,
13“Tsono Ine ndidzakupsinjani
14Munthu waliwiro sadzatha kuthawa,
15Munthu wa uta sadzalimbika,
16Ngakhale asilikali olimba mtima kwambiri