1Mawu a Amosi, mmodzi mwa anthu oweta nkhosa ku Tekowa. Zimene iye anaona mʼmasomphenya zokhudza Israeli patatsala zaka ziwiri kuti chivomerezi chichitike, nthawi imene Uziya anali mfumu ya Yuda ndipo Yeroboamu mwana wa Yowasi anali mfumu ya Israeli.
2Amosi anati:
3Yehova akuti,
4Ine ndidzatumiza moto pa nyumba ya Hazaeli
5Ndidzathyola chipata cha Damasiko;
6Yehova akuti,
7ndidzatumiza moto pa makoma a Gaza
8Ndidzawononga mfumu ya ku Asidodi
9Yehova akuti,
10Ine ndidzatumiza moto pa makoma a Turo
11Yehova akuti,
12Ine ndidzatumiza moto pa Temani
13Yehova akuti,
14Ine ndidzayatsa moto pa makoma a ku Raba
15Mfumu yawo idzatengedwa kupita ku ukapolo,