We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Amosi 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

Amosi Amosi 2 →

1Mawu a Amosi, mmodzi mwa anthu oweta nkhosa ku Tekowa. Zimene iye anaona mʼmasomphenya zokhudza Israeli patatsala zaka ziwiri kuti chivomerezi chichitike, nthawi imene Uziya anali mfumu ya Yuda ndipo Yeroboamu mwana wa Yowasi anali mfumu ya Israeli.

2Amosi anati:

3Yehova akuti,

4Ine ndidzatumiza moto pa nyumba ya Hazaeli

5Ndidzathyola chipata cha Damasiko;

6Yehova akuti,

7ndidzatumiza moto pa makoma a Gaza

8Ndidzawononga mfumu ya ku Asidodi

9Yehova akuti,

10Ine ndidzatumiza moto pa makoma a Turo

11Yehova akuti,

12Ine ndidzatumiza moto pa Temani

13Yehova akuti,

14Ine ndidzayatsa moto pa makoma a ku Raba

15Mfumu yawo idzatengedwa kupita ku ukapolo,

Amosi Amosi 2 →