We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Amosi 3

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Amosi 2 Amosi Amosi 4 →

1Inu Aisraeli, imvani mawu awa amene Yehova wayankhula kutsutsana nanu, kutsutsana ndi banja lonse limene analitulutsa mu Igupto:

2“Inu nokha ndi amene ndinakusankhani

3Kodi anthu awiri nʼkuyendera limodzi

4Kodi mkango umabangula mʼnkhalango

5Kodi mbalame nʼkutera pa msampha

6Kodi pamene lipenga la nkhondo lalira mu mzinda,

7Zoonadi Ambuye Yehova sachita kanthu

8Mkango wabangula,

9Lengezani zimenezi ku nyumba zaufumu za ku Asidodi

10“Iwo sadziwa kuchita zolungama,

11Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akunena izi:

12Yehova akuti,

13“Imvani izi ndipo mupereke umboni wotsutsa nyumba ya Yakobo,” akutero Ambuye, Yehova Mulungu Wamphamvuzonse.

14“Pa tsiku limene ndidzalange Israeli chifukwa cha machimo ake,

15Ndidzagwetsa nyumba ya pa nthawi yozizira

← Amosi 2 Amosi Amosi 4 →