1Inu Aisraeli, imvani mawu awa amene Yehova wayankhula kutsutsana nanu, kutsutsana ndi banja lonse limene analitulutsa mu Igupto:
2“Inu nokha ndi amene ndinakusankhani
3Kodi anthu awiri nʼkuyendera limodzi
4Kodi mkango umabangula mʼnkhalango
5Kodi mbalame nʼkutera pa msampha
6Kodi pamene lipenga la nkhondo lalira mu mzinda,
7Zoonadi Ambuye Yehova sachita kanthu
8Mkango wabangula,
9Lengezani zimenezi ku nyumba zaufumu za ku Asidodi
10“Iwo sadziwa kuchita zolungama,
11Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akunena izi:
12Yehova akuti,
13“Imvani izi ndipo mupereke umboni wotsutsa nyumba ya Yakobo,” akutero Ambuye, Yehova Mulungu Wamphamvuzonse.
14“Pa tsiku limene ndidzalange Israeli chifukwa cha machimo ake,
15Ndidzagwetsa nyumba ya pa nthawi yozizira