We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Zekariya 9

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Zekariya 8 Zekariya Zekariya 10 →

1Mawu a Yehova odzudzula dziko la Hadiraki

2ndiponso mzinda wa Hamati, umene ukuchita malire ndi dzikoli,

3Ndipo Turo anadzimangira linga;

4Taonani Ambuye adzamulanda chuma chakecho

5Mzinda wa Asikeloni udzaona zimenezi, nʼkuchita mantha;

6Mu Asidodi mudzakhala mlendo,

7Ndidzachotsa nyama ya magazi mʼkamwa mwawo,

8Koma Ine ndidzalondera Nyumba yanga

9Sangalala kwambiri, iwe mwana wamkazi wa Ziyoni!

10Ndidzachotsa magaleta ankhondo ku Efereimu

11Tsono kunena za iwe, chifukwa cha magazi a pangano lako ndi Ine,

12Bwererani ku malo anu otetezedwa, inu amʼndende achiyembekezo;

13Ndidzakoka Yuda monga ndimakokera uta wanga,

14Pamenepo Yehova adzaonekera kwa anthu ake;

15ndipo Yehova Wamphamvuzonse adzawateteza.

16Tsiku limenelo Yehova Mulungu wawo adzawapulumutsa

17Taonani chikoka ndi kukongola kwawo!

← Zekariya 8 Zekariya Zekariya 10 →