1Pemphani mvula kwa Yehova pa nthawi yamphukira;
2Mafano amayankhula zachinyengo,
3“Ine ndawakwiyira kwambiri abusa,
4Mu Yuda mudzachokera mwala wapangodya,
5Onse pamodzi adzakhala ngati ngwazi zankhondo
6“Ndidzalimbitsa nyumba ya Yuda
7Aefereimu adzakhala ngati ankhondo amphamvu
8Ndidzaliza mluzu
9Ndinawamwaza pakati pa mitundu ina ya anthu,
10Ndidzawabweretsa kuchokera ku Igupto
11Adzawoloka nyanja ya masautso;
12Ndidzalimbitsa iwo mwa Yehova