1Imvani Inu Yehova pempho langa lachilungamo;
2Kusalakwa kwanga kuchokera kwa inu;
3Ngakhale Inu mutafufuza mtima wanga ndi kundisanthula usiku,
4Kunena za ntchito za anthu,
5Mayendedwe anga akhazikika pa njira zanu;
6Ine ndikuyitana Inu, Mulungu wanga, pakuti mudzandiyankha;
7Onetsani kudabwitsa kwa chikondi chanu chachikulu,
8Mundisunge ine ngati mwanadiso;
9kuchoka kwa oyipa amene amandizinga ine,
10Iwo amatseka mitima yawo yopanda chifundo,
11Andisaka, tsopano andizungulira
12Iwo ali ngati mkango wofuna nyama;
13Dzukani Yehova, mulimbane nawo ndipo muwagwetse pansi;
14Inu Yehova, pulumutseni ndi dzanja lanu kwa anthu otere,
15Ndipo ine mʼchilungamo ndidzaona nkhope yanu;