We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 17

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 16 Masalimo Masalimo 18 →

1Imvani Inu Yehova pempho langa lachilungamo;

2Kusalakwa kwanga kuchokera kwa inu;

3Ngakhale Inu mutafufuza mtima wanga ndi kundisanthula usiku,

4Kunena za ntchito za anthu,

5Mayendedwe anga akhazikika pa njira zanu;

6Ine ndikuyitana Inu, Mulungu wanga, pakuti mudzandiyankha;

7Onetsani kudabwitsa kwa chikondi chanu chachikulu,

8Mundisunge ine ngati mwanadiso;

9kuchoka kwa oyipa amene amandizinga ine,

10Iwo amatseka mitima yawo yopanda chifundo,

11Andisaka, tsopano andizungulira

12Iwo ali ngati mkango wofuna nyama;

13Dzukani Yehova, mulimbane nawo ndipo muwagwetse pansi;

14Inu Yehova, pulumutseni ndi dzanja lanu kwa anthu otere,

15Ndipo ine mʼchilungamo ndidzaona nkhope yanu;

← Masalimo 16 Masalimo Masalimo 18 →