1Tamandani Yehova.
2amene mumatumikira mʼnyumba ya Yehova,
3Tamandani Yehova, pakuti Yehova ndi wabwino;
4Pakuti Yehova wasankha Yakobo kuti akhale wake,
5Ndikudziwa kuti Yehova ndi wamkulu,
6Yehova amachita chilichonse chimene chimamukomera,
7Iye amatulutsa mitambo kuchokera ku malekezero a dziko lapansi,
8Anakantha ana oyamba kubadwa a Igupto,
9Iye anatumiza zizindikiro zozizwitsa ndi zodabwitsa pakati pako, iwe Igupto,
10Iye anakantha mitundu yambiri ya anthu
11Sihoni mfumu ya Aamori,
12ndipo anapereka dziko lawo ngati cholowa,
13Dzina lanu, Inu Yehova, ndi losatha mpaka muyaya,
14Pakuti Yehova adzaonetsa kuti anthu ake ngosalakwa,
15Mafano a mitundu ya anthu ndi siliva ndi golide,
16Pakamwa ali napo koma sayankhula
17makutu ali nawo, koma sakumva
18Iwo amene amapanga mafanowo adzakhala ngati mafanowo,
19Inu nyumba ya Israeli, tamandani Yehova;
20Inu nyumba ya Levi, tamandani Yehova;
21Wodalitsika ndi Yehova kuchokera mʼZiyoni,