1“Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga,”
2“Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga,
3Anthu otipula analima pa msana panga
4Koma Yehova ndi wolungama;
5Onse amene amadana ndi Ziyoni
6Akhale ngati udzu womera pa denga la nyumba,
7sungadzaze manja a owumweta
8Odutsa pafupi asanene kuti,