1Odala ndi onse amene amaopa Yehova,
2Udzadya chipatso cha ntchito yako;
3Mkazi wako adzakhala ngati mpesa wobereka
4Ameneyu ndiye munthu wodalitsidwa
5Yehova akudalitse kuchokera mʼZiyoni
6ndipo ukhale ndi moyo kuti udzaone zidzukulu zako.
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja
1Odala ndi onse amene amaopa Yehova,
2Udzadya chipatso cha ntchito yako;
3Mkazi wako adzakhala ngati mpesa wobereka
4Ameneyu ndiye munthu wodalitsidwa
5Yehova akudalitse kuchokera mʼZiyoni
6ndipo ukhale ndi moyo kuti udzaone zidzukulu zako.