We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 128

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 127 Masalimo Masalimo 129 →

1Odala ndi onse amene amaopa Yehova,

2Udzadya chipatso cha ntchito yako;

3Mkazi wako adzakhala ngati mpesa wobereka

4Ameneyu ndiye munthu wodalitsidwa

5Yehova akudalitse kuchokera mʼZiyoni

6ndipo ukhale ndi moyo kuti udzaone zidzukulu zako.

← Masalimo 127 Masalimo Masalimo 129 →