1Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni,
2Monga mapiri azungulira Yerusalemu,
3Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala
4Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino,
5Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota,
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja
1Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni,
2Monga mapiri azungulira Yerusalemu,
3Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala
4Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino,
5Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota,