1Akanapanda kukhala mbali yathu Yehova,
2akanapanda kukhala mbali yathu Yehova,
3iwo atatipsera mtima,
4chigumula chikanatimiza,
5madzi a mkokomo
6Atamandike Yehova,
7Moyo wathu wawonjoka ngati mbalame
8Thandizo lathu lili mʼdzina la Yehova
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja
1Akanapanda kukhala mbali yathu Yehova,
2akanapanda kukhala mbali yathu Yehova,
3iwo atatipsera mtima,
4chigumula chikanatimiza,
5madzi a mkokomo
6Atamandike Yehova,
7Moyo wathu wawonjoka ngati mbalame
8Thandizo lathu lili mʼdzina la Yehova