We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 118

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 117 Masalimo Masalimo 119 →

1Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino;

2Israeli anene kuti:

3Banja la Aaroni linene kuti,

4Iwo amene amaopa Yehova anene kuti:

5Ndili mʼmasautso anga ndinalirira Yehova,

6Yehova ali nane; sindidzachita mantha.

7Yehova ali nane; Iye ndiye thandizo langa.

8Nʼkwabwino kuthawira kwa Yehova

9Nʼkwabwino kuthawira kwa Yehova

10Anthu a mitundu yonse anandizinga,

11Anandizinga mbali zonse,

12Anandizinga ngati njuchi,

13Anandikankha uku ndi uko ndipo ndinali pafupi kugwa,

14Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga;

15Mfuwu wachimwemwe ndi chipambano

16Dzanja lamanja la Yehova latukulidwa mmwamba

17Sindidzafa koma ndidzakhala ndi moyo

18Yehova wandilanga koopsa,

19Tsekulireni zipata zachilungamo,

20Ichi ndicho chipata cha Yehova

21Ndidzakuyamikani chifukwa Inu munandiyankha;

22Mwala umene amisiri omanga nyumba anawukana

23Yehova ndiye wachita zimenezi

24Lero ndiye tsiku limene Yehova walipanga;

25Inu Yehova, tipulumutseni;

26Wodala amene akubwera mʼdzina la Yehova.

27Yehova ndi Mulungu,

28Inu ndinu Mulungu wanga, ndipo ndidzakuyamikani;

29Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino;

← Masalimo 117 Masalimo Masalimo 119 →