1Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino;
2Israeli anene kuti:
3Banja la Aaroni linene kuti,
4Iwo amene amaopa Yehova anene kuti:
5Ndili mʼmasautso anga ndinalirira Yehova,
6Yehova ali nane; sindidzachita mantha.
7Yehova ali nane; Iye ndiye thandizo langa.
8Nʼkwabwino kuthawira kwa Yehova
9Nʼkwabwino kuthawira kwa Yehova
10Anthu a mitundu yonse anandizinga,
11Anandizinga mbali zonse,
12Anandizinga ngati njuchi,
13Anandikankha uku ndi uko ndipo ndinali pafupi kugwa,
14Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga;
15Mfuwu wachimwemwe ndi chipambano
16Dzanja lamanja la Yehova latukulidwa mmwamba
17Sindidzafa koma ndidzakhala ndi moyo
18Yehova wandilanga koopsa,
19Tsekulireni zipata zachilungamo,
20Ichi ndicho chipata cha Yehova
21Ndidzakuyamikani chifukwa Inu munandiyankha;
22Mwala umene amisiri omanga nyumba anawukana
23Yehova ndiye wachita zimenezi
24Lero ndiye tsiku limene Yehova walipanga;
25Inu Yehova, tipulumutseni;
26Wodala amene akubwera mʼdzina la Yehova.
27Yehova ndi Mulungu,
28Inu ndinu Mulungu wanga, ndipo ndidzakuyamikani;
29Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino;