1Nawa mawu a mfumu Lemueli wa ku Massa amene anamuphunzitsa amayi ake:
2Nʼchiyani mwana wanga? Nʼchiyani mwana wa mʼmimba mwanga?
3Usapereke mphamvu yako kwa akazi.
4Iwe Lemueli si choyenera kwa mafumu,
5kuopa kuti akamwa adzayiwala malamulo a dziko,
6Perekani chakumwa choledzeretsa kwa amene ali pafupi kufa,
7amwe kuti ayiwale umphawi wawo
8Yankhula mʼmalo mwa amene sangathe kudziyankhulira okha.
9Yankhula ndi kuweruza mwachilungamo.
10Kodi mkazi wangwiro angathe kumupeza ndani?
11Mtima wa mwamuna wake umamukhulupirira
12Masiku onse a moyo wake
13Iye amafunafuna ubweya ndi thonje;
14Iye ali ngati sitima zapamadzi za anthu amalonda,
15Iye amadzuka kusanache kwenikweni;
16Iye amalingalira za munda ndi kuwugula;
17Iye amavala zilimbe
18Iye amaona kuti malonda ake ndi aphindu,
19Iye amadzilukira thonje
20Iye amachitira chifundo anthu osauka
21Iye saopa kuti banja lake lifa ndi kuzizira pa nyengo yachisanu;
22Iye amadzipangira yekha zoyala pa bedi pake;
23Mwamuna wake ndi wodziwika pa chipata cha mzinda,
24Iye amasoka nsalu zabafuta nazigulitsa;
25Mphamvu ndi ulemu zimakhala ngati chovala chake;
26Iye amayankhula mwanzeru,
27Iye amayangʼanira makhalidwe a anthu a pa banja lake
28Ana ake amamunyadira ndipo amamutcha kuti wodala;
29“Pali akazi ambiri amene achita zinthu zopambana
30Nkhope yachikoka ndi yonyenga, ndipo kukongola nʼkosakhalitsa;
31Mupatseni mphotho chifukwa cha zimene iye wachita