1“Ansembe inu, imvani izi!
2Owukira azama mʼmoyo wakupha,
3Ndimadziwa zonse za Efereimu;
4“Ntchito zawo siziwalola
5Kudzikuza kwa Israeli kwakhala umboni womutsutsa;
6Pamene adzapita ndi nkhosa zawo ndi ngʼombe zawo
7Iwo ndi osakhulupirika kwa Yehova;
8“Womba lipenga mu Gibeya,
9Efereimu adzasanduka bwinja
10Atsogoleri a Yuda ali ngati anthu
11Efereimu waponderezedwa,
12Ine ndili ngati njenjete kwa Efereimu,
13“Efereimu ataona nthenda yake,
14Pakuti Ine ndidzakhala ngati mkango kwa Efereimu.
15Ndipo ndidzabwerera ku malo anga