1Inu Aisraeli, imvani mawu a Yehova,
2Muli kutemberera kokha, kunama ndi kupha.
3Chifukwa chake dziko likulira
4“Koma wina asapeze mnzake chifukwa,
5Mumapunthwa usana ndi usiku
6Anthu anga akuwonongeka chifukwa chosadziwa.
7Ansembe ankati akachuluka
8Amalemererapo pa machimo a anthu anga
9Ndipo zidzakhala motere: zochitikira anthu ena, zidzachitikiranso ansembe.
10“Iwo azidzadya koma sadzakhuta;
11ku zachiwerewere,
12za anthu anga.
13Amapereka nsembe pamwamba pa mapiri
14“Ine sindidzalanga ana anu aakazi
15“Ngakhale umachita chigololo, iwe Israeli,
16Aisraeli ndi nkhutukumve,
17Efereimu waphathana ndi mafano;
18Ngakhale pamene zakumwa zawo zatha,
19Adzachotsedwa ndi kamvuluvulu