We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yobu 16

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yobu 15 Yobu Yobu 17 →

1Pamenepo Yobu anayankha kuti,

2“Ndinamvapo zambiri monga zimenezi;

3Kodi mawu anu ochulukawo adzatha?

4Inenso ndikanatha kuyankhula monga inu,

5Ndipo mawu a pakamwa panga akanakulimbikitsani;

6“Koma ine ndikati ndiyankhule ululu wanga sukuchepa;

7Ndithudi, Inu Mulungu mwanditha mphamvu;

8Inu mwandimanga ndipo kundimangako kwakhala umboni;

9Mulungu amabwera kwa ine mwankhanza ndipo amadana nane,

10Anthu amatsekula pakamwa pawo kundikuwiza;

11Mulungu wandipereka kwa anthu ochita zoyipa

12Ine ndinali pamtendere, koma Mulungu ananditswanya;

13anthu ake oponya mauta andizungulira.

14Akundivulaza kawirikawiri,

15“Ndasokerera chiguduli pa thupi langa

16Maso anga afiira ndi kulira,

17komatu manja anga sanachite zachiwawa

18“Iwe dziko lapansi, usakwirire magazi anga;

19Ngakhale tsopano mboni yanga ili kumwamba;

20Wondipembedzera ndi bwenzi langa,

21iye, mʼmalo mwanga, amamudandaulira Mulungu

22“Pakuti sipapita zaka zambiri

← Yobu 15 Yobu Yobu 17 →