1Yehova, Inu mumakhala wokhoza nthawi zonse
2Inu munawadzala ndipo anamera mizu;
3Koma Inu Yehova, ine mumandidziwa;
4Kodi dziko lidzakhala likulirabe mpaka liti
5Yehova anayankha kuti, “Ngati kukutopetsa kuthamanga pamodzi ndi anthu
6Ngakhale abale ako
7“Ine ndawasiya anthu anga;
8Anthu amene ndinawasankha
9Anthu anga amene ndinawasankha
10Abusa ambiri anawononga munda wanga wa mpesa,
11Unawusandutsadi chipululu.
12Anthu onse owononga abalalikira
13Anthu anafesa tirigu koma anatuta minga;
14“Anthu oyipa oyandikana ndi anthu anga Aisraeli, akuwalanda Aisraeliwo dziko, cholowa chimene ndinawapatsa. Nʼchifukwa chake ndidzawachotsa mʼdziko limenelo, ndipo ndidzachotsa banja la Yuda pakati pawo.
15Komabe nditawachotsa, ndidzawachitiranso chifundo, ndipo ndidzabwezera aliyense cholowa chake ndi dziko lake.
16Ndipo ngati iwo adzaphunzira bwino njira za anthu anga ndi kulumbira mʼdzina langa, namanena kuti, ‘Pali Yehova wamoyo,’ monga iwo anaphunzitsira anthu anga kulumbira mʼdzina la Baala, Ine ndidzawakhazikitsa pakati pa anthu anga.
17Koma ngati mtundu wina uliwonse sudzamvera, Ine ndidzawuchotsa ndi kuwuwonongeratu,” akutero Yehova.