We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yobu 38

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yobu 37 Yobu Yobu 39 →

1Apo Yehova anamuyankha Yobu mʼkamvuluvulu. Ndipo anati:

2“Kodi uyu ndani amene akusokoneza uphungu wanga

3Onetsa chamuna;

4“Kodi unali kuti pamene ndinkayika maziko a dziko lapansi?

5Ndani amene analemba malire ake? Ndithudi iwe ukudziwa!

6Kodi maziko ake anawakumba potani,

7pamene nyenyezi za kummawa zinkayimba pamodzi

8“Kodi ndani amene anatsekera nyanja pamene inkalengedwa,

9pamene ndinasandutsa mitambo kukhala chovala chake

10pamene ndinayilembera malire ake

11Pamene ndinati, ‘Ufike mpaka apa ndipo usapitirire

12“Kodi chibadwire chako unalamulapo dzuwa kuti lituluke mmawa,

13kuti kuwalako kuwunikire dziko lonse lapansi

14Chifukwa cha kuwala kwa usana mapiri ndi zigwa zimaonekera bwino ngati zilembo za chidindo pa mtapo;

15Kuwala kwa dzuwako sikuwafikira anthu oyipa,

16“Kodi unayendapo pansi penipeni pa nyanja

17Kodi anakuonetsapo zipata za imfa?

18Kodi kukula kwa dziko lapansi umakudziwa?

19“Kodi njira yopita kumene kumakhala kuwala ili kuti?

20Kodi iwe ungathe kuziperekeza kwawoko zimenezi?

21Ndithu, iwe ukuyidziwa, poti paja nthawi imeneyo nʼkuti utabadwa kale!

22“Kodi unalowamo mʼnyumba zosungira chisanu chowundana

23zimene ndazisungira nthawi ya mavuto

24Kodi umadziwa njira ya kumene kumachokera chingʼaningʼani

25Kodi ndani amene amakonza ngalande za mvula,

26kuthirira madzi dziko limene sikukhala munthu,

27kukhutitsa nthaka yowuma yagwaa

28Kodi mvula ili ndi abambo ake?

29Kodi madzi owundana anawabereka ndani?

30pamene madzi amawuma gwaa ngati mwala,

31“Kodi iwe ungayimitse kuyenda kwa nyenyezi?

32Kodi ungathe kuwongolera nyenyezi pa nyengo yake

33Kodi malamulo a mlengalenga umawadziwa?

34“Kodi iwe ungathe kulamula mitambo

35Kodi ungathe kutumiza zingʼaningʼani kuti zingʼanime?

36Kodi ndani anayika nzeru mu mtima,

37Wanzeru ndani amene angathe kuwerenga mitambo?

38pamene fumbi limasanduka matope,

39“Kodi ndani amawusakira chakudya mkango waukazi

40pamene ili khale mʼmapanga mwawo

41Kodi amamupatsa khwangwala chakudya chake ndani

← Yobu 37 Yobu Yobu 39 →