1Ndipo Elihu anawonjeza kunena kuti,
2“Kodi mukuganiza kuti mukukhoza?
3Komanso inu mukufunsa kuti, ‘Kodi phindu langa nʼchiyani,
4“Ine ndikufuna ndikuyankheni inu
5Yangʼanani kumwamba ndipo muone
6Inuyo mukachimwa, Iye zimamukhudza motani?
7Ngati inu ndinu wolungama, mumamupatsa Iyeyo chiyani?
8Kuyipa kwanu kumangokhudza anthu ngati inuyo,
9“Anthu akufuwula chifukwa cha kuzunzidwa;
10Koma palibe amene akunena kuti, ‘Kodi ali kuti Mulungu, Mlengi wanga,
11amene amatiphunzitsa kupambana nyama za dziko lapansi
12Iye sayankha pamene anthu akufuwulira kwa Iye
13Ndithu, Mulungu samva kupempha kwawo kopanda pake;
14Ndipo ndi bodza lalikulu kunena kuti
15ndiye tsono popeza kuti ukali wake sukupereka chilango,
16abambo Yobu mumangoyankhula zopandapake,