1Pamenepo Yobu anayankha kuti,
2“Wamuthandizadi munthu wopanda mphamvu!
3Wapereka malangizo kwa munthu amene alibe nzeru!
4Kodi wakuthandiza ndani kuti uyankhule mawu awa?
5“Mizimu ya anthu akufa ikunjenjemera pansi pa madzi,
6Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu;
7Mulungu anayala thambo la kumpoto pa phompho;
8Amasunga madzi ambiri mʼmitambo yake,
9Iye amaphimba mwezi wowala,
10Mulungu anawalembera madzi malire wonga uta,
11Mizati yochirikiza mitambo yakumwamba imanjenjemera,
12Ndi mphamvu zake anatontholetsa nyanja;
13Ndi mpweya wake anayeretsa zamumlengalenga,
14Zimenezi ndi pangʼono chabe mwa ntchito yake;