We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yobu 17

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yobu 16 Yobu Yobu 18 →

1“Mtima wanga wasweka,

2Ndithudi, anthu ondiseka andizungulira;

3“Inu Mulungu, patseni chikole chimene mukufuna.

4Inu mwatseka maganizo awo kuti asamvetse zinthu;

5Ngati munthu apereka mnzake chifukwa cha chuma,

6“Mulungu wandisandutsa chisudzo chochiseka aliyense,

7Mʼmaso mwanga mwada ndi chisoni;

8Anthu olungama akudabwa nazo zimenezi;

9Komabe anthu olungama adzasunga njira zawo,

10“Tsono bwerani nonsenu, bwerezaninso mawu anuwo,

11Masiku anga atha, zimene ndinakonza zalephereka,

12Anthu awa amasandutsa usiku kukhala usana,

13Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda,

14ngati ndinena kwa dzenje la manda ‘ndinu abambo anga,’

15tsono chiyembekezo changa chili kuti?

16Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse,

← Yobu 16 Yobu Yobu 18 →