We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yobu 10

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yobu 9 Yobu Yobu 11 →

1“Ine ndatopa nawo moyo wanga;

2Ndidzati kwa Mulungu wanga: Musandiweruze kuti ndine wolakwa,

3Kodi mumakondwera mukamandizunza,

4Kodi maso anu ali ngati a munthu?

5Kodi masiku anu ali ngati masiku a munthu,

6kuti Inu mufufuze zolakwa zanga

7ngakhale mukudziwa kuti sindine wolakwa

8“Munandiwumba ndi kundipanga ndi manja anu.

9Kumbukirani kuti munandipanga ndi dothi,

10Suja munapatsa abambo anga mphamvu zoti andibale,

11Munandikuta ndi khungu ndi mnofu

12Munandipatsa moyo ndi kundionetsa chifundo chanu,

13“Koma izi ndi zimene munabisa mu mtima mwanu,

14Kuti ngati ndingachimwe mudzakhala mukundipenyetsetsa

15Ngati ndili wolakwa, tsoka langa!

16Ndipo ndikatukula mutu wanga, Inu mumandisaka ngati mkango

17Mumabweretsa mboni zatsopano potsutsana nane

18“Chifukwa chiyani Inu munalola kuti ndibadwe?

19Ndikanapanda kubadwa,

20Kodi masiku anga owerengeka sali pafupi kutha?

21ndisanapite ku malo amene munthu sabwererako

22ku dziko la mdima wandiweyani

← Yobu 9 Yobu Yobu 11 →