1Anthu amene anali ndi nkhawa, sadzakhalanso otaya mtima. Masiku amakedzana Mulungu ananyozetsa dziko la Zebuloni ndi dziko la Nafutali, koma kutsogolo kuno dera lonse la Galileya, limene lili dziko la anthu a mitundu ina, kuyambira ku nyanja yayikulu, mʼmbali mwa Yorodani, adzalisandutsa laulemu.
2Anthu oyenda mu mdima
3Inu mwauchulukitsa mtundu wanu
4Monga munachitira pogonjetsa Amidiyani,
5Nsapato iliyonse ya munthu wankhondo,
6Chifukwa mwana watibadwira,
7Ulamuliro ndi mtendere wake
8Ambuye atumiza mawu otsutsa Yakobo;
9Anthu onse okhala mu
10“Ngakhale njerwa zagumuka,
11Koma Yehova wadzutsa adani kuti alimbane nawo
12Asiriya ochokera kummawa ndi Afilisti ochokera kumadzulo ndipo
13Koma anthu sanabwerere kwa amene anawakantha uja,
14Choncho Yehova adzadula mutu wa Israeli pamodzi ndi mchira womwe,
15mutuwo ndiye akuluakulu ndi olemekezeka,
16Amene amatsogolera anthuwa ndiwo amawasocheretsa,
17Nʼchifukwa chake Ambuye adzakondwera nawo achinyamata,
18Ndithu kuyipa kwa anthuwo kumayaka ngati moto;
19Dziko lidzatenthedwa ndi ukali wa Yehova Wamphamvuzonse,
20Kudzanja lamanja adzapeza chakudya nʼkudya,
21Manase adzadya Efereimu ndipo Efereimu adzadya Manase;