1Ndidzamuyimbira bwenzi langa
2Anatipula nachotsa miyala yonse
3“Tsopano, inu amene mumakhala mu Yerusalemu ndi inu anthu a ku Yuda,
4Kodi nʼchiyaninso china chimene ndikanachitira munda wanga wa mpesa
5Tsopano ndikuwuzani
6Ndidzawusandutsa tsala,
7Munda wamphesa wa Yehova Wamphamvuzonse
8Tsoka kwa inu amene mumangokhalira kulumikiza nyumba,
9Yehova Wamphamvuzonse wayankhula ine ndikumva kuti,
10Munda wamphesa wa maekala khumi udzatulutsa vinyo wodzaza mbiya imodzi,
11Tsoka kwa iwo amene amadzuka mmamawa
12Pa maphwando awo pamakhala azeze, apangwe,
13Motero anthu anga adzatengedwa ukapolo
14Nʼchifukwa chake ku manda sikukhuta
15Ndipo munthu aliyense adzatsitsidwa,
16Koma Yehova Wamphamvuzonse adzalemekezedwa chifukwa cha chiweruzo chake cholungama.
17Tsono nkhosa zidzadya pamenepo ngati pabusa pawo;
18Tsoka kwa amene amadzikokera tchimo ndi zingwe zachinyengo,
19amene amanena kuti, “Yehova afulumire,
20Tsoka kwa amene zoyipa amaziyesa zabwino
21Tsoka kwa amene amadziona ngati anzeru
22Tsoka kwa zidakwa zimene zimayika mtima pa vinyo
23amene amamasula olakwa chifukwa cha chiphuphu
24Nʼchifukwa chake monga momwe moto umawonongera chiputu
25Nʼchifukwa chake mkwiyo wa Yehova wayakira anthu ake;
26Yehova wakweza mbendera kuyitana mtundu wa anthu akutali,
27Palibe ndi mmodzi yemwe amene akutopa kapena kupunthwa,
28Mivi yawo ndi yakuthwa,
29Kufuwula kwawo kuli ngati kubangula kwa mkango,
30Tsiku limenelo mitundu ya anthu idzabangula